Rute 2:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Naomi anali naye mbale wa mwamuna wake, ndiye munthu mwini chuma chambiri wa banja la Elimeleki; dzina lake ndiye Bowazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Naomi anali naye mbale wa mwamuna wake, ndiye munthu mwini chuma chambiri wa banja la Elimeleki; dzina lake ndiye Bowazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Naomi anali ndi wachibale wake wachuma kwambiri, wa m'banja la malemu mwamuna wake uja Elimeleki, dzina lake Bowazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Naomi anali ndi mʼbale wake wolemera kwambiri wochokera ku banja la mwamuna wake Elimeleki, dzina lake Bowazi. Onani mutuwo |