Rute 1:9 - Buku Lopatulika9 Yehova akuloleni mupeze mpumulo yense m'nyumba ya mwamuna wake. Nawapsompsona, nakweza iwo mau ao nalira misozi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Yehova akuloleni mupeze mpumulo yense m'nyumba ya mwamuna wake. Nawapsompsona, nakweza iwo mau ao nalira misozi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chauta akuthandizeni kuti mupeze pokhala, ndipo aliyense mwa inu akwatiwe.” Pompo adaŵampsompsona. Koma iwo adayamba kulira mokweza, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Yehova akuthandizeni kuti aliyense wa inu apeze pokhala pabwino komanso mwamuna.” Kenaka anawapsompsona koma awiriwo analira mokweza. Onani mutuwo |