Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Rute 1:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo ananena naye, Iai, koma tidzapita nanu kwa anthu a kwanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo ananena naye, Iai, koma tidzapita nanu kwa anthu a kwanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 nauza Naomiyo kuti, “Iyai, ife tipita nao kwa anthu akwanu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ndipo anati kwa Naomi, “Ife tipita nawo kwa anthu akwanu.”

Onani mutuwo Koperani




Rute 1:10
6 Mawu Ofanana  

Ine ndine wakuyanjana nao onse akukuopani, ndi iwo akusamalira malangizo anu.


Za oyera mtima okhala padziko lapansi, iwo ndiwo omveka mbiri, mwa iwowo muli chikondwero changa chonse.


Atero Yehova wa makamu: Kudzachitika masiku awo amuna khumi adzagwira, ndiwo a manenedwe onse a amitundu, inde adzagwira mkawo wa munthu ali Myuda, ndi kuti, Tidzamuka nanu, pakuti tamva kuti Mulungu ali ndi inu.


Nati Naomi, Bwererani, ana anga, mudzatsagana nane bwanji? Ngati ndili nao m'mimba mwanga ana aamuna ena kuti akhale amuna anu?


Natuluka iye kumene anakhalako ndi apongozi ake awiri pamodzi naye; nanka ulendo wao kubwerera ku dziko la Yuda.


Yehova akuloleni mupeze mpumulo yense m'nyumba ya mwamuna wake. Nawapsompsona, nakweza iwo mau ao nalira misozi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa