Rute 1:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo ananena naye, Iai, koma tidzapita nanu kwa anthu a kwanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo ananena naye, Iai, koma tidzapita nanu kwa anthu a kwanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 nauza Naomiyo kuti, “Iyai, ife tipita nao kwa anthu akwanu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo anati kwa Naomi, “Ife tipita nawo kwa anthu akwanu.” Onani mutuwo |