Rute 1:11 - Buku Lopatulika11 Nati Naomi, Bwererani, ana anga, mudzatsagana nane bwanji? Ngati ndili nao m'mimba mwanga ana aamuna ena kuti akhale amuna anu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Nati Naomi, Bwererani, ana anga, mudzatsagana nane bwanji? Ngati ndili nao m'mimba mwanga ana amuna ena kuti akhale amuna anu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Koma Naomi adaŵauza kuti, “Pepani ana anga, bwererani kwanu. Chifukwa chiyani mukufuna kupita nao? Kodi mukuganiza kuti ndingathe kubala ana ena aamuna, kuti adzakhale amuna anu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Koma Naomi anati, “Bwererani kwanu ana anga. Chifukwa chiyani mukufuna kupita ndi ine? Kodi ine ndingaberekenso ana ena kuti akhale amuna anu? Onani mutuwo |