Oweruza 1:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Yuda ananena ndi Simeoni mkulu wake, Kwera nane ku gawo langa kuti tiwathire nkhondo Akanani; ndipo inenso ndidzamuka nawe ku gawo lako. Namuka naye Simeoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Yuda ananena ndi Simeoni mkulu wake, Kwera nane ku gawo langa kuti tiwathire nkhondo Akanani; ndipo inenso ndidzamuka nawe ku gawo lako. Namuka naye Simeoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pamenepo Ayuda adauza abale ao, anthu a fuko la Simeoni, kuti, “Tiyeni tipite limodzi m'dziko limene Chauta adagaŵira ife, kuti tikamenyane ndi Akanani. Pambuyo pake nafenso tidzapita nanu limodzi m'dziko limene adagaŵira inu.” Choncho Asimeoni adatsakana nawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Choncho Ayuda anawuza abale awo a fuko la Simeoni kuti, “Bwerani tipitire limodzi mʼdziko limene tapatsidwa kuti tikamenyane ndi Akanaani. Ifenso tidzapita nanu mʼdziko limene anakugawirani.” Ndipo Asimeoni anapita nawo. Onani mutuwo |