Oweruza 1:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Yuda atakwera, Yehova anapereka Akanani ndi Aperizi m'dzanja lao, ndipo anakantha a iwowa anthu zikwi khumi ku Bezeki. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Yuda atakwera, Yehova anapereka Akanani ndi Aperizi m'dzanja lao, ndipo anakantha a iwowa anthu zikwi khumi ku Bezeki. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Onsewo adapita, ndipo Chauta adapereka Akananiwo m'manja mwao pamodzi ndi Aperizi omwe. Ndipo adagonjetsa anthu 10,000 ku Bezeki. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Choncho Ayuda ananyamuka, ndipo Yehova anapereka Akanaani ndi Aperezi mʼmanja mwawo. Ndipo anapha anthu 10,000 ku Bezeki. Onani mutuwo |