Obadiya 1:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo amuna anu amphamvu adzatenga nkhawa, Temani iwe, kuti onse aonongeke m'phiri la Edomu, ndi kuphedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo amuna anu amphamvu adzatenga nkhawa, Temani iwe, kuti onse aonongeke m'phiri la Edomu, ndi kuphedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ngwazi za ku Temani zidzachita mantha, ankhondo onse adzaphedwa ku mapiri a Esau. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ankhondo ako, iwe Temani, adzachita mantha, ndipo aliyense amene ali mʼphiri la Esau adzaphedwa pa nkhondo. Onani mutuwo |