Obadiya 1:8 - Buku Lopatulika8 Ati Yehova, Kodi sindidzaononga tsiku lija anzeru mwa Edomu, ndi luntha m'phiri la Esau? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ati Yehova, Kodi sindidzaononga tsiku lija anzeru mwa Edomu, ndi luntha m'phiri la Esau? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chauta akuti, “Nthaŵi imeneyo ndidzaononga anzeru onse a ku Edomu, ndidzathetsa kuchenjera konse kwa zidzukulu za Esau. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Yehova akunena kuti, “Tsiku limenelo, kodi sindidzawononga anthu onse anzeru a ku Edomu, anthu odziwa zinthu mʼmapiri a Esau? Onani mutuwo |