Obadiya 1:10 - Buku Lopatulika10 Chifukwa cha chiwawa unamchitira mphwako Yakobo, udzakutidwa ndi manyazi, nudzaonongeka kunthawi yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Chifukwa cha chiwawa unamchitira mphwako Yakobo, udzakutidwa ndi manyazi, nudzaonongeka kunthawi yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Aedomu inu, chifukwa cha zankhanza zimene mudachita abale anu, zidzukulu za Yakobe, adzakuchititsani manyazi ndi kukuwonongani mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Chifukwa cha nkhanza zimene unachitira mʼbale wako Yakobo, udzakhala wamanyazi; adzakuwononga mpaka muyaya. Onani mutuwo |