Obadiya 1:2 - Buku Lopatulika2 Taona, ndakuika wamng'ono mwa amitundu; unyozedwa kwambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Taona, ndakuika wamng'ono mwa amitundu; unyozedwa kwambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chauta akuuza Aedomu kuti, “Ndithu ndidzakutsitsani kotheratu, anthu a mitundu yonse adzakunyozani kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Taona, ndidzakuchepetsani pakati pa anthu a mitundu ina; udzanyozedwa kwambiri. Onani mutuwo |