Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Obadiya 1:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 “Taona, ndidzakuchepetsani pakati pa anthu a mitundu ina; udzanyozedwa kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

2 Taona, ndakuika wamng'ono mwa amitundu; unyozedwa kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Taona, ndakuika wamng'ono mwa amitundu; unyozedwa kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Chauta akuuza Aedomu kuti, “Ndithu ndidzakutsitsani kotheratu, anthu a mitundu yonse adzakunyozani kwambiri.

Onani mutuwo Koperani




Obadiya 1:2
9 Mawu Ofanana  

Yehova Wamphamvuzonse anakonza zimenezi kuti athetse kunyada kwawo ndi kutsitsa anthu otchuka a pa dziko lapansi.


“Ndidzakuchepetsani pakati pa anthu a mitundu ina. Mudzakhala anthu onyozeka pakati pa anthu.


Udzakhala ufumu wotsika kwambiri kupambana maufumu ena onse ndipo sudzadzitukumula pakati pa mitundu ina. Ndidzawufowoketsa kwambiri kotero kuti sudzathanso kulamulira mitundu ya anthu.


Ndipo mdani wanga adzaona zimenezi nadzagwidwa ndi manyazi, iye amene anandifunsa kuti, “Ali kuti Yehova Mulungu wako?” Ndidzaona kugonjetsedwa kwake ndi maso anga; ngakhale tsopano adzaponderezedwa ngati matope mʼmisewu.


Edomu adzagonjetsedwa; Seiri, mdani wake, adzawonongedwa koma mphamvu za Israeli zidzachuluka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa