Obadiya 1:17 - Buku Lopatulika17 Koma m'phiri la Ziyoni mudzakhala opulumuka, ndipo lidzakhala lopatulika; ndi a nyumba ya Yakobo adzakhala nazo zolowa zao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma m'phiri la Ziyoni mudzakhala opulumuka, ndipo lidzakhala lopatulika; ndi a nyumba ya Yakobo adzakhala nazo zolowa zao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 “Koma pa phiri la Ziyoni padzakhala ena opulumuka, ndipo phirilo lidzakhala loyera. Pamenepo fuko la Yakobe lidzalandira choloŵa chakechake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Koma pa Phiri la Ziyoni padzakhala chipulumutso; phirilo lidzakhala lopatulika, ndipo nyumba ya Yakobo idzalandira cholowa chake. Onani mutuwo |