Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 9:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo Mose ananena ndi ana a Israele, kuti achite Paska.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo Mose ananena ndi ana a Israele, kuti achite Paska.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Choncho Mose adauza Aisraele kuti azichita Paska.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Choncho Mose anawuza Aisraeli kuti azichita Paska,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 9:4
3 Mawu Ofanana  

Pamenepo Mose anaitana akulu onse a Israele, nanena nao, Pitani, dzitengereni anaankhosa monga mwa mabanja anu, nimuphere Paska.


Tsiku lakhumi ndi chinai la mweziwo, madzulo, muziuchita, pa nyengo yake yoikidwa; muuchite monga mwa malemba ake onse, ndi maweruzo ake onse.


Ndipo anachita Paska mwezi woyamba, tsiku lakhumi ndi chinai la mweziwo, madzulo m'chipululu cha Sinai; monga mwa zonse Yehova adauza Mose, momwemo ana a Israele anachita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa