Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 7:41 - Buku Lopatulika

41 ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

41 ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Selumiele mwana wa Zurishadai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

41 Ndipo zoperekera nsembe yachiyanjano zinali ng'ombe ziŵiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu ndi anaankhosa asanu amphongo a chaka chimodzi. Zimenezi ndizo zinali zopereka za Selumiele mwana a Zurishadai.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

41 ngʼombe ziwiri, nkhosa zisanu, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Selumieli mwana wa Zurisadai.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:41
4 Mawu Ofanana  

Wa Simeoni, Selumiele mwana wa Zurishadai.


Ndipo iwo akumanga mahema ao poyandikizana naye ndiwo a fuko la Simeoni; ndi kalonga wa ana a Simeoni ndiye Selumiele mwana wa Zurishadai.


tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo;


Tsiku lachisanu ndi chimodzi kalonga wa ana a Gadi, Eliyasafu mwana wa Deuwele:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa