Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 7:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono Chauta adauza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Yehova anawuza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:4
3 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo ananyamulira likasa la Mulungu pa galeta watsopano, atalitulutsa m'nyumba ya Abinadabu, ili pachitunda, ndipo Uza ndi Ahiyo ana a Abinadabu anayendetsa ng'ombe za pa galeta watsopanoyo.


anadza nacho chopereka chao pamaso pa Yehova, magaleta ophimbika asanu ndi mmodzi, ndi kalonga awiru anapereka galeta ndi kalonga mmodzi ng'ombe imodzi; nabwera nazo pakhomo pa chihema.


Uzilandira kwa iwo, kuti zikhale zakuchitira ntchito ya chihema chokomanako; nuzipereke kwa Alevi, yense monga mwa ntchito yake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa