Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 7:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Yehova anawuza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

4 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Tsono Chauta adauza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:4
3 Mawu Ofanana  

Iwo anayika Bokosi la Mulungu pa ngolo yatsopano nachoka nalo ku nyumba ya Abinadabu, imene inali pa phiri. Uza ndi Ahiyo ana a Abinadabu ndiwo ankayendetsa ngolo yatsopanoyo,


Anabweretsa zopereka zawo pamaso pa Yehova: ngolo zophimbidwa zisanu ndi imodzi ndiponso ngʼombe zothena khumi ndi ziwiri. Mtsogoleri mmodzi ngʼombe yothena imodzi ndipo atsogoleri awiri ngolo imodzi. Izi anazipereka ku chihema.


“Ulandire zimenezi kwa iwo kuti zigwire ntchito ku tenti ya msonkhano. Uzipereke kwa Alevi, aliyense monga mwa ntchito yake.”


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa