Numeri 6:8 - Buku Lopatulika8 Masiku onse a kusala kwake akhala wopatulikira kwa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Masiku onse a kusala kwake akhala wopatulikira kwa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Munthuyo ndi wopatulikira Chauta masiku onse a kudzipereka kwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Munthuyo ndi wopatulika masiku onse odzipereka kwake kwa Yehova. Onani mutuwo |