Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 6:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Munthuyo ndi wopatulika masiku onse odzipereka kwake kwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

8 Masiku onse a kusala kwake akhala wopatulikira kwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Masiku onse a kusala kwake akhala wopatulikira kwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Munthuyo ndi wopatulikira Chauta masiku onse a kudzipereka kwake.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 6:8
5 Mawu Ofanana  

Ngakhale abambo ake kapena amayi ake kapena mchimwene wake kaya mchemwali wake atamwalira, asadzidetse pokhudza mitembo yawo chifukwa kulumbira kwake kwa kudzipatula yekha kwa Yehova kuli pamutu pake.


“Ngati munthu wina afa mwadzidzidzi pafupi naye ndi kudetsa tsitsi lake loperekedwalo, amete mutu wake pa tsiku lodziyeretsa, tsiku lachisanu ndi chiwiri.


Ndinapempha mwana uyu, ndipo Yehova wandipatsa chimene ndinamupempha.


Ndiye tsopano ine ndikumupereka kwa Yehova. Pa moyo wake wonse adzakhala wa Yehova.” Ndipo onse anapembedza Yehova kumeneko.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa