Numeri 6:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo chilamulo cha Mnaziri, atatha masiku a kusala kwake ndi ichi: azidza naye ku khomo la chihema chokomanako; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo chilamulo cha Mnaziri, atatha masiku a kusala kwake ndi ichi: azidza naye ku khomo la chihema chokomanako; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 “Lamulo la Mnaziri pamene nthaŵi ya kudzipereka kwake yatha, nali: abwere naye pakhomo pa chihema chamsonkhano, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 “Tsono ili ndi lamulo la Mnaziri pamene nthawi yodzipatula kwake yatha: Abwere naye pa khomo la tenti ya msonkhano. Onani mutuwo |