Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 5:30 - Buku Lopatulika

30 kapena pamene mtima wansanje umgwira mwamuna, ndipo achitira mkazi wake nsanje; pamenepo aziika mkazi pamaso pa Yehova, ndipo wansembe amchitire chilamulo ichi chonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 kapena pamene mtima wansanje umgwira mwamuna, ndipo achitira mkazi wake nsanje; pamenepo aziika mkazi pamaso pa Yehova, ndipo wansembe amchitire chilamulo ichi chonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 kapena mwamuna akayamba kuchitira mkazi wake nsanje ndipo akumganizira zoipa. Mwamunayo amuimike mkazi wake pamaso pa Chauta, ndipo wansembe amchitire monga momwe lamulo likunenera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 kapena pamene maganizo a nsanje abwera kwa mwamuna wake chifukwa chokayikira mkazi wakeyo. Wansembe azitenga mkazi wotere ndi kumuyimiritsa pamaso pa Yehova ndipo agwiritse ntchito lamulo lonseli kwa mkaziyo.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 5:30
3 Mawu Ofanana  

ndipo ukamgwira mwamuna mtima wansanje, kuti achitire nsanje mkazi wake, popeza wadetsedwa; kapena ukamgwira mtima wansanje, kuti amchitire mkazi wake nsanje angakhale sanadetsedwe;


Ichi ndi chilamulo cha nsanje, pamene mkazi, pokhala naye mwamuna wake, ampatukira nadetsedwa;


Mwamunayo ndiye wosachita mphulupulu, koma mkazi uyo asenze mphulupulu yake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa