Numeri 5:26 - Buku Lopatulika26 Wansembe atengekonso nsembe yaufa wodzala manja, chikumbutso chake, nachitenthe paguwa la nsembe; ndipo atatero amwetse mkazi madziwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Wansembe atengekonso nsembe yaufa wodzala manja, chikumbutso chake, nachitenthe pa guwa la nsembe; ndipo atatero amwetse mkazi madziwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Wansembe atapeko ufa wa dzanja limodzi kuti ukhale chikumbutso ndi kuutenthera pa guwa. Pambuyo pake apatse mkaziyo madzi aja kuti amwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Tsono wansembeyo atapeko ufa dzanja limodzi kuti ukhale wachikumbutso ndi kuwutentha pa guwa lansembe. Atatha izi, amwetse mkaziyo madzi aja. Onani mutuwo |