Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 4:41 - Buku Lopatulika

41 Amenewo ndiwo owerengedwa a mabanja a ana a Geresoni, onse akutumikira m'chihema chokomanako, adawawerenga Mose ndi Aroni monga mwa mau a Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

41 Amenewo ndiwo owerengedwa a mabanja a ana a Geresoni, onse akutumikira m'chihema chokomanako, adawawerenga Mose ndi Aroni monga mwa mau a Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

41 Chimenechi ndicho chinali chiŵerengero cha anthu a m'banja a Ageresoni, amene ankatumikira m'chihema chamsonkhano, amene Mose ndi Aroni adaŵaŵerenga, monga momwe Chauta adaalamulira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

41 Ichi chinali chiwerengero cha Ageresoni mwa mabanja awo amene ankatumikira ku tenti ya msonkhano. Mose ndi Aaroni anawawerenga monga mwa lamulo la Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 4:41
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anawawerenga monga mwa mau a Yehova, monga adamuuza.


owerengedwa ao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi limodzi kudza makumi atatu.


Ndipo owerengedwa a mabanja a ana a Merari, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao,


Anawawerenga monga mwa mau a Yehova ndi dzanja la Mose, onse monga mwa ntchito zao, ndi monga mwa akatundu ao; anawawerenga monga momwe Yehova adauza Mose.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa