Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 4:41 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

41 Ichi chinali chiwerengero cha Ageresoni mwa mabanja awo amene ankatumikira ku tenti ya msonkhano. Mose ndi Aaroni anawawerenga monga mwa lamulo la Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

41 Amenewo ndiwo owerengedwa a mabanja a ana a Geresoni, onse akutumikira m'chihema chokomanako, adawawerenga Mose ndi Aroni monga mwa mau a Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

41 Amenewo ndiwo owerengedwa a mabanja a ana a Geresoni, onse akutumikira m'chihema chokomanako, adawawerenga Mose ndi Aroni monga mwa mau a Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

41 Chimenechi ndicho chinali chiŵerengero cha anthu a m'banja a Ageresoni, amene ankatumikira m'chihema chamsonkhano, amene Mose ndi Aroni adaŵaŵerenga, monga momwe Chauta adaalamulira.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 4:41
4 Mawu Ofanana  

Choncho Mose anawawerenga potsatira zomwe Yehova anamulamulira.


atawawerenga mwa mafuko ndi mabanja awo, anali 2,630.


Amerari anawawerenga monga mwa mafuko ndi mabanja awo.


Aliyense anamupatsa ntchito ndi kumuwuza choti anyamule monga mwa lamulo la Yehova kudzera mwa Mose. Anawawerenga chomwechi potsata zimene Yehova analamula Mose.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa