Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 4:40 - Buku Lopatulika

40 owerengedwa ao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi limodzi kudza makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 owerengedwa ao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi limodzi kudza makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Chiŵerengero chao chidakwanira 2,630 potsata mabanja ao ndiponso banja la makolo ao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 atawawerenga mwa mafuko ndi mabanja awo, anali 2,630.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 4:40
3 Mawu Ofanana  

Ndipo kalonga wa akalonga a Alevi ndiye Eleazara mwana wa Aroni wansembeyo; ndiye aziyang'anira osunga udikiro wa pamalo opatulika.


kuyambira a zaka makumi atatu ndi mphambu kufikira a zaka makumi asanu, onse akulowa utumikiwu, kuti agwire ntchito m'chihema chokomanako,


Amenewo ndiwo owerengedwa a mabanja a ana a Geresoni, onse akutumikira m'chihema chokomanako, adawawerenga Mose ndi Aroni monga mwa mau a Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa