Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 4:36 - Buku Lopatulika

36 ndipo owerengedwa ao monga mwa mabanja ao ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi awiri kudza makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 ndipo owerengedwa ao monga mwa mabanja ao ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi awiri kudza makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 ndipo chiŵerengero chao chidakwanira 2,750 potsata mabanja ao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 atawawerenga mwa mafuko awo, anali 2,750.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 4:36
2 Mawu Ofanana  

kuyambira a zaka makumi atatu ndi mphambu kufikira a zaka makumi asanu, onse akulowa utumikiwu, kuti agwire ntchito m'chihema chokomanako;


Awa ndi owerengedwa a mabanja a Akohati, onse akutumikira m'chihema chokomanako, amene Mose ndi Aroni anawawerenga monga mwa mau a Yehova mwa dzanja la Mose.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa