Numeri 4:35 - Buku Lopatulika35 kuyambira a zaka makumi atatu ndi mphambu kufikira a zaka makumi asanu, onse akulowa utumikiwu, kuti agwire ntchito m'chihema chokomanako; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 kuyambira a zaka makumi atatu ndi mphambu kufikira a zaka makumi asanu, onse akulowa utumikiwu, kuti agwire ntchito m'chihema chokomanako; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Adaŵaŵerenga anthuwo kuyambira a zaka makumi atatu mpaka a zaka makumi asanu, onse amene ankatha kutumikira m'chihema chamsonkhano, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Aamuna onse a zaka makumi atatu mpaka makumi asanu amene anabwera kudzagwira ntchito ku tenti ya msonkhano, Onani mutuwo |