Numeri 4:18 - Buku Lopatulika18 Musamasadza fuko la mabanja a Akohati kuwachotsa pakati pa Alevi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Musamasadza fuko la mabanja a Kohati kuwachotsa pakati pa Alevi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 “Musalole kuti a m'banja la Kohati aonongeke pakati pa Alevi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 “Onetsetsani kuti mabanja a fuko la Kohati asachotsedwe kwa Alevi. Onani mutuwo |