Numeri 4:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo azichotsa mapulusa paguwa la nsembe, ndi kuyala pa ilo nsalu yofiirira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo azichotsa mapulusa pa guwa la nsembe, ndi kuyala pa ilo nsalu yofiirira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ataye phulusa lapaguwa, ndipo ayalepo nsalu yofiira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 “Azichotsa phulusa la pa guwa lansembe lamkuwa ndi kuyalapo nsalu yapepo pamwamba pake. Onani mutuwo |