Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 4:13 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 “Azichotsa phulusa la pa guwa lansembe lamkuwa ndi kuyalapo nsalu yapepo pamwamba pake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

13 Ndipo azichotsa mapulusa paguwa la nsembe, ndi kuyala pa ilo nsalu yofiirira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo azichotsa mapulusa pa guwa la nsembe, ndi kuyala pa ilo nsalu yofiirira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Ataye phulusa lapaguwa, ndipo ayalepo nsalu yofiira.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 4:13
7 Mawu Ofanana  

Anapanga zovala za ansembe, zovala potumikira ku malo wopatulika pogwiritsa ntchito nsalu ya mtundu wa mtambo, yapepo ndi yofiira. Anapanganso zovala zopatulika za Aaroni monga momwe Yehova analamulira Mose.


ndiponso zovala zolukidwa zovala potumikira kumalo opatulika, zovala zopatulika za wansembe, Aaroni pamodzi ndi za ana ake aamuna pamene akutumikira monga ansembe.


Kenaka aziyikapo zipangizo zonse zogwiritsira ntchito potumikira pa guwa, kuphatikizapo miphika yowotchera nyama, mafoloko otengera nyama, zowolera phulusa ndi mbale zowazira magazi pa guwa lansembe ndipo pamwamba pake aziyalapo zikopa za akatumbu ndi kuziyika mʼzonyamulira zake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa