Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 4:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo achimange ndi chipangizo zake zonse m'chophimba cha zikopa za akatumbu, ndi kuziika pa chonyamulira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo achimange ndi chipangizo zake zonse m'chophimba cha zikopa za akatumbu, ndi kuziika pa chonyamulira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Ndipo achiike pamodzi ndi zipangizo zake zonse m'thumba la zikopa zambuzi, ndi kuchiika pa chonyamulira chake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Kenaka achikulunge pamodzi ndi zipangizo zake zonse mʼzikopa za akatumbu ndi kuchiyika pa chonyamulira chake.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 4:10
6 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipanga choikaponyali cha golide woona; choikapocho chisulidwe mapangidwe ake, tsinde lake ndi thupi lake; zikho zake, mitu yake, ndi maluwa ake zikhale zochokera m'mwemo;


ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Ndipo paguwa la nsembe lagolide aziyala nsalu ya madzi, naliphimbe ndi chophimba cha zikopa za akatumbu, ndi kupisako mphiko zake.


Natenge zipangizo zake zonse za utumiki, zimene atumikira nazo m'malo opatulika, nazimange m'nsalu yamadzi, ndi kuziphimba ndi chophimba cha zikopa za akatumbu, ndi kuziika pachonyamulira.


ndi kuikapo chophimba cha zikopa za akatumbu; ndi kuyalapo nsalu yamadzi yeniyeni, ndi kupisako mphiko zake.


Ndipo atenge nsalu yamadzi, ndi kuphimba choikaponyali younikira, ndi nyali zake, ndi mbano zake, ndi zoolera zake, ndi zotengera zake zonse za mafuta zogwira nazo ntchito yake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa