Numeri 4:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo achimange ndi chipangizo zake zonse m'chophimba cha zikopa za akatumbu, ndi kuziika pa chonyamulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo achimange ndi chipangizo zake zonse m'chophimba cha zikopa za akatumbu, ndi kuziika pa chonyamulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndipo achiike pamodzi ndi zipangizo zake zonse m'thumba la zikopa zambuzi, ndi kuchiika pa chonyamulira chake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kenaka achikulunge pamodzi ndi zipangizo zake zonse mʼzikopa za akatumbu ndi kuchiyika pa chonyamulira chake. Onani mutuwo |