Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 36:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo mwana wamkazi yense wa mafuko a ana a Israele, wakukhala nacho cholowa, akwatibwe ndi wina wa banja la fuko la kholo lake, kuti ana a Israele akhale nacho yense cholowa cha makolo ake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo mwana wamkazi yense wa mafuko a ana a Israele, wakukhala nacho cholowa, akwatibwe ndi wina wa banja la fuko la kholo lake, kuti ana a Israele akhale nacho yense cholowa cha makolo ake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Mkazi aliyense amene alandira choloŵa m'fuko lililonse la Aisraele, akwatiwe ndi ana a abale a bambo wao. Mwisraele aliyense adzalandira choloŵa cha makolo ake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Mwana wamkazi aliyense amene adzalandira cholowa cha dziko la fuko lililonse la Israeli ayenera kukwatiwa ndi munthu wa fuko la abambo ake.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 36:8
2 Mawu Ofanana  

Nafa Eleazara wopanda ana aamuna, koma ana aakazi ndiwo; ndi asuweni ao ana a Kisi anawatenga akhale akazi ao.


Motero cholowa cha ana a Israele sichidzanka ku fuko ndi fuko, pakuti mafuko a ana a Israele adzamamatira lonse ku cholowa chakechake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa