Numeri 36:12 - Buku Lopatulika12 Anakwatibwa mwa mabanja a ana a Manase mwana wa Yosefe; ndipo cholowa chao chinakhala m'fuko la banja la atate wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Anakwatibwa mwa mabanja a ana a Manase mwana wa Yosefe; ndipo cholowa chao chinakhala m'fuko la banja la atate wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Adakwatiwa ndi a m'mabanja a ana a Manase mwana wa Yosefe, ndipo choloŵa chao chidakhalabe m'fuko la bambo wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Anakwatiwa mʼmafuko a zidzukulu za Manase mwana wa Yosefe, ndipo cholowa chawo chinakhalabe mʼfuko la abambo awo. Onani mutuwo |