Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 36:11 - Buku Lopatulika

11 popeza Mala, Tiriza, ndi Hogila, ndi Milika, ndi Nowa, ana aakazi a Zelofehadi, anakwatibwa ndi ana aamuna a abale a atate wao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 popeza Mala, Tiriza, ndi Hogila, ndi Milika, ndi Nowa, ana akazi a Zelofehadi, anakwatibwa ndi ana amuna a abale a atate wao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Mala, Tiriza, Hogola, Milika ndi Nowa, ana aakazi a Zelofehadi, adakwatiwa ndi ana a abale a bambo wao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Ana aakazi a Zelofehadi amene ndi Mahila, Tiriza, Hogila, Milika ndi Nowa, anakwatiwa ndi asuweni awo a ku mbali ya abambo awo.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 36:11
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Zelofehadi mwana wa Hefere analibe ana aamuna, koma ana aakazi ndiwo; ndipo maina a ana aakazi a Zelofehadi ndiwo Mala ndi Nowa, Hogila, Milika ndi Tiriza.


Pamenepo anayandikiza ana aakazi a Zelofehadi mwana wa Hefere, ndiye mwana wa Giliyadi, ndiye mwana wa Makiri, ndiye mwana wamwamuna wa Manase, wa mabanja a Manase mwana wa Yosefe; ndipo maina a ana ake aakazi ndiwo, Mala, Nowa, Hogila ndi Milika ndi Tiriza.


Monga Yehova adalamulira Mose, momwemo ana aakazi a Zelofehadi anachita;


Anakwatibwa mwa mabanja a ana a Manase mwana wa Yosefe; ndipo cholowa chao chinakhala m'fuko la banja la atate wao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa