Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 36:10 - Buku Lopatulika

10 Monga Yehova adalamulira Mose, momwemo ana aakazi a Zelofehadi anachita;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Monga Yehova adalamulira Mose, momwemo ana akazi a Zelofehadi anachita;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Ana aakazi a Zelofehadi adachitadi zomwe Mulungu adalamula Mose.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Choncho ana aakazi a Zelofehadi anachita monga Yehova analamulira Mose.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 36:10
9 Mawu Ofanana  

Ku Yuda komwe kunali dzanja la Mulungu lakuwapatsa mtima umodzi, kuchita chowauza mfumu ndi akulu mwa mau a Yehova.


Ndipo ana onse a Israele anachita monga Yehova adawalamulira Mose ndi Aroni, momwemo anachita.


Ndipo Mose ananena ndi ana a Israele, ndipo anatulutsa wotembererayo kunja kwa chigono, namponya miyala. Ndipo ana a Israele anachita monga Yehova adauza Mose.


Momwemo ana a Israele anachita monga mwa zonse Yehova adauza Mose; anachita momwemo.


popeza Mala, Tiriza, ndi Hogila, ndi Milika, ndi Nowa, ana aakazi a Zelofehadi, anakwatibwa ndi ana aamuna a abale a atate wao.


Motero cholowa cha ana a Israele sichidzanka ku fuko ndi fuko, pakuti mafuko a ana a Israele adzamamatira lonse ku cholowa chakechake.


ndi kuwaphunzitsa, asunge zinthu zonse zimene ndinakulamulani inu; ndipo onani, Ine ndili pamodzi ndi inu masiku onse, kufikira chimaliziro cha nthawi ya pansi pano.


Ndipo anayandikira pamaso pa Eleazara wansembe, ndi pamaso pa Yoswa mwana wa Nuni, ndi pamaso pa akalonga, ndi kuti, Yehova analamulira Mose atipatse cholowa pakati pa abale athu; chifukwa chake anawapatsa monga mwa lamulo la Yehova, cholowa pakati pa abale a atate wao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa