Numeri 36:13 - Buku Lopatulika13 Awa ndi malamulo ndi maweruzo, amene Yehova analamulira ana a Israele ndi dzanja la Mose m'zidikha za Mowabu pa Yordani ku Yeriko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Awa ndi malamulo ndi maweruzo, amene Yehova analamulira ana a Israele ndi dzanja la Mose m'zidikha za Mowabu pa Yordani ku Yeriko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ameneŵa ndiwo malamulo ndi malangizo amene Chauta adalamula Aisraele kudzera mwa Mose. Adaperekedwa m'zigwa za Mowabu, pafupi ndi mtsinje wa Yordani ku Yeriko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Awa ndi malamulo ndi malangizo amene Yehova anapereka kwa Aisraeli kupyolera mwa Mose ku chigwa cha Mowabu mʼmbali mwa Yorodani, ku Yeriko. Onani mutuwo |