Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 35:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo mabusa a mizindayo, imene muipereke kwa Alevi ndiwo a mikono chikwi chimodzi kuyambira kulinga kufikira kunja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo mabusa a midziyo, imene muipereke kwa Alevi ndiwo a mikono chikwi chimodzi kuyambira kulinga kufikira kunja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Mabusa a mizindayo amene mudzapatse Aleviwo, adzayambire ku khoma la mzinda, adzatuluke kunja mamita 450, kuzungulira mzindawo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 “Malo a msipu a mudziwo amene mudzawapatse Aleviwo, adzayambire ku khoma la mudzi ndipo adzatuluke kunja mamita 450, kuzungulira mudziwo.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 35:4
2 Mawu Ofanana  

Ndipo mizinda ndiyo yokhalamo iwowa; ndi mabusa akhale a ng'ombe zao, ndi zoweta zao, inde nyama zao zonse.


Ndipo muyese kunja kwa mzinda, mbali ya kum'mawa mikono zikwi ziwiri, ndi mbali ya kumwera mikono zikwi ziwiri, ndi mbali ya kumadzulo mikono zikwi ziwiri, ndi mbali ya kumpoto mikono zikwi ziwiri; ndi mzindawo pakati; ndiwo mabusa a kumizinda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa