Numeri 35:11 - Buku Lopatulika11 muikire mizinda ikukhalireni mizinda yopulumukirako; kuti wakupha mnzake wosati dala athawireko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 muikire midzi ikukhalireni midzi yopulumukirako; kuti wakupha mnzake wosati dala athawireko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 mupatule mizinda ina kuti ikhale mizinda yanu yothaŵirako, kumene munthu wopha mnzake mwangozi azithaŵirako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 sankhani midzi ina kuti ikhale mizinda yanu yopulumukirako, kumene munthu wopha munthu wina mwangozi angathawireko. Onani mutuwo |