Numeri 33:49 - Buku Lopatulika49 Ndipo anamanga pa Yordani, kuyambira ku Beteyesimoti kufikira ku Abele-Sitimu m'zidikha za Mowabu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 Ndipo anamanga pa Yordani, kuyambira ku Beteyesimoti kufikira ku Abele-Sitimu m'zidikha za Mowabu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 Adamanga mahema ao pafupi ndi mtsinje wa Yordani kuyambira ku Beteyesimoti mpaka ku Abele-Sitimu, m'zigwa za Mowabu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 Ali ku zigwa za Mowabu anamanga mʼmbali mwa Yorodani kuchokera ku Beti-Yesimoti mpaka ku Abeli-Sitimu. Onani mutuwo |