Numeri 33:50 - Buku Lopatulika50 Ndipo Yehova ananena ndi Mose m'zidikha za Mowabu pa Yordani ku Yeriko, nati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 Ndipo Yehova ananena ndi Mose m'zidikha za Mowabu pa Yordani ku Yeriko, nati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Chauta adauza Mose m'zigwa za Mowabu pafupi ndi mtsinje wa Yordani, kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Pa zigwa za Mowabu, mʼmbali mwa Yorodani moyangʼanana ndi ku Yeriko, Yehova anawuza Mose kuti, Onani mutuwo |