Numeri 33:48 - Buku Lopatulika48 Nachokera ku mapiri a Abarimu, nayenda namanga m'zidikha za Mowabu pa Yordani ku Yeriko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Nachokera ku mapiri a Abarimu, nayenda namanga m'zidikha za Mowabu pa Yordani ku Yeriko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Adanyamuka ku mapiri a Abarimu, nakamanga mahema ao ku zigwa za ku Mowabu, pafupi ndi mtsinje wa Yordani ku Yeriko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Atachoka ku mapiri a Abarimu anakamanga ku zigwa za Mowabu mʼmbali mwa Yorodani moyangʼanana ndi Yeriko. Onani mutuwo |