Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 33:40 - Buku Lopatulika

40 Ndipo Mkanani, mfumu ya Aradi, wakukhala kumwera m'dziko la Kanani, anamva za kudza kwao kwa ana a Israele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Ndipo Mkanani, mfumu ya Aradi, wakukhala kumwera m'dziko la Kanani, anamva za kudza kwao kwa ana a Israele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Mfumu ya ku Aradi, Mkanani amene ankakhala m'dziko la Kanani, adamva kuti Aisraele akubwera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 Mfumu ya Akanaani ya ku Aradi yomwe inkakhala ku Negevi kummwera kwa Kanaani, inamva kuti Aisraeli akubwera.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 33:40
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Abramu anayenda ulendo wake, nayendayenda kunka kumwera.


Ndipo Aroni ndiye wa zaka zana limodzi mphambu makumi awiri kudza zitatu pakufa iye m'phiri la Hori.


Ndipo anachokera kuphiri la Hori, nayenda namanga mu Zalimona.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa