Numeri 33:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo Aroni ndiye wa zaka zana limodzi mphambu makumi awiri kudza zitatu pakufa iye m'phiri la Hori. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo Aroni ndiye wa zaka zana limodzi mphambu makumi awiri kudza zitatu pakufa iye m'phiri la Hori. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Aroniyo anali wa zaka 123 za kubadwa, pamene adamwalira pa phiri la Hori. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Aaroni anamwalira pa phiri la Hori ali ndi zaka 123. Onani mutuwo |