Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 33:18 - Buku Lopatulika

18 Nachokera ku Hazeroti, nayenda namanga mu Ritima.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Nachokera ku Hazeroti, nayenda namanga m'Ritima.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Adanyamuka ku Hazeroti, nakamanga mahema ao ku Ritima.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Atachoka ku Heziroti anakamanga ku Ritima.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 33:18
3 Mawu Ofanana  

Ndipo atatero anthuwo ananka ulendo wao kuchokera ku Hazeroti, namanga mahema ao m'chipululu cha Parani.


Nachokera ku Kibroti-Hatava, nayenda namanga mu Hazeroti.


Nachokera ku Ritima, nayenda namanga mu Rimoni-Perezi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa