Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 33:14 - Buku Lopatulika

14 Nachokera ku Alusi, nayenda namanga mu Refidimu; kumeneko kunalibe madzi kuti anthu amwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Nachokera ku Alusi, nayenda namanga m'Refidimu; kumeneko kunalibe madzi kuti anthu amwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Adanyamuka ku Alusi, nakamanga mahema ao ku Refidimu kumene kunalibe madzi akumwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Atachoka ku Alusi anakamanga misasa yawo ku Refidimu, kumene kunalibe madzi woti anthu ndi kumwa.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 33:14
3 Mawu Ofanana  

Pakuti anachoka ku Refidimu, nalowa m'chipululu cha Sinai, namanga tsasa m'chipululumo; ndipo Israele anamanga tsasa pamenepo pandunji paphirilo.


Nachokera ku Dofika, nayenda namanga mu Alusi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa