Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 33:13 - Buku Lopatulika

13 Nachokera ku Dofika, nayenda namanga mu Alusi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Nachokera ku Dofika, nayenda namanga m'Alusi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Adanyamuka ku Dofika, nakamanga mahema ao ku Alusi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Atachoka ku Dofika anakamanga misasa yawo ku Alusi.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 33:13
2 Mawu Ofanana  

Nachokera ku chipululu cha Sini, nayenda namanga mu Dofika.


Nachokera ku Alusi, nayenda namanga mu Refidimu; kumeneko kunalibe madzi kuti anthu amwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa