Numeri 33:1 - Buku Lopatulika1 Maulendo a ana a Israele amene anatuluka m'dziko la Ejipito monga mwa makamu ao, ndi dzanja la Mose ndi Aroni, ndi awa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Maulendo a ana a Israele amene anatuluka m'dziko la Ejipito monga mwa makamu ao, ndi dzanja la Mose ndi Aroni, ndi awa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pamene Aisraele adatuluka m'dziko la Ejipito m'magulu a mafuko ao, Mose ndi Aroni akuŵatsogolera, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Malo otsatirawa ndi omwe Aisraeli anayima pa maulendo awo atatuluka mʼdziko la Igupto mʼmagulu awo motsogozedwa ndi Mose ndi Aaroni. Onani mutuwo |