Numeri 32:42 - Buku Lopatulika42 Ndipo Noba ananka nalanda Kenati, ndi midzi yake, nautcha Noba, dzina lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Ndipo Noba ananka nalanda Kenati, ndi milaga yake, nautcha Noba, dzina lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Noba adapita kukalanda mzinda wa Kenati pamodzi ndi midzi yake, ndipo adautcha Noba, kutengera dzina lake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Ndipo Noba analanda Kenati ndi midzi yozungulira ndi kuyitcha Noba, kutengera dzina la iye mwini. Onani mutuwo |