Numeri 32:38 - Buku Lopatulika38 ndi Nebo, ndi Baala-Meoni (anasintha maina ao), ndi Sibima; ndipo anaitcha mizinda adaimanga ndi maina ena. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 ndi Nebo, ndi Baala-Meoni (anasintha maina ao), ndi Sibima; ndipo anaitcha midzi adaimanga ndi maina ena. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Nebo, Baala-Meoni (dzina ili lidasinthidwa) ndi Sibima. Mizinda imene adamangayo adaitcha maina ena. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Nebo ndi Baala-Meoni (mayina awa anasinthidwa) ndi Sibima. Anapereka mayina ku mizinda ina yomwe anamangayo. Onani mutuwo |