Numeri 32:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo ana a Rubeni anamanga Hesiboni, ndi Eleyale, ndi Kiriyataimu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo ana a Rubeni anamanga Hesiboni, ndi Eleyale, ndi Kiriyataimu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Ana a Rubeni adamanga mizinda ya Hesiboni. Eleyale, Kiriyataimu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Ndipo Arubeni anamanga Hesiboni, Eleali, Kiriataimu, Onani mutuwo |