Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 32:37 - Buku Lopatulika

37 Ndipo ana a Rubeni anamanga Hesiboni, ndi Eleyale, ndi Kiriyataimu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Ndipo ana a Rubeni anamanga Hesiboni, ndi Eleyale, ndi Kiriyataimu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Ana a Rubeni adamanga mizinda ya Hesiboni. Eleyale, Kiriyataimu,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Ndipo Arubeni anamanga Hesiboni, Eleali, Kiriataimu,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 32:37
10 Mawu Ofanana  

Chaka chakhumi ndi chinai ndipo anadza Kedorilaomere ndi mafumu amene anali naye, nawakantha Arefaimu mu Asiteroti-Karanaimu, ndi Azuzimu mu Hamu, ndi Aemimu mu Savekiriyataimu,


Ndi Hesiboni afuula zolimba, ndi Eleyale; mau ao amveka, ngakhale ku Yahazi; chifukwa chake amuna ankhondo a Mowabu afuula zolimba; moyo wake wanthunthumira m'kati mwake.


Za Mowabu. Atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele: Tsoka Nebo! Pakuti wapasuka; Kiriyataimu wachitidwa manyazi, wagwidwa; linga la pamtunda lachitidwa manyazi lapasudwa.


Kuyambira kufuula kwa Hesiboni mpaka ku Eleyale, mpaka ku Yahazi anakweza mau, kuyambira pa Zowari mpaka ku Horonaimu, ku Egilati-Selisiya; pakuti pamadzi a ku Nimurimu komwe padzakhala mabwinja.


chifukwa chake taona ndidzatsegula pambali pake pa Mowabu kuyambira kumizinda, kumizinda yake yokhala mphepete, yokometsetsa ya m'dziko, Beteyesimoti, Baala-Meoni, ndi Kiriyataimu,


Chifukwa chake iwo akunena mophiphiritsa akuti, Idzani ku Hesiboni, mzinda wa Sihoni umangike, nukhazikike.


Ataroti, ndi Diboni, ndi Yazere, ndi Nimira, ndi Hesiboni, ndi Eleyale, ndi Sibima, ndi Nebo, ndi Beoni,


ndi Betenimura, ndi Beteharani: mizinda ya m'malinga, ndi makola a zoweta.


ndi Nebo, ndi Baala-Meoni (anasintha maina ao), ndi Sibima; ndipo anaitcha mizinda adaimanga ndi maina ena.


ndi Kiriyataimu, ndi Sibima, ndi Zeretisahara, m'phiri la kuchigwa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa