Numeri 32:27 - Buku Lopatulika27 koma anyamata anu adzaoloka, yense wokonzekera ndi zankhondo pamaso pa Yehova kunkhondo, monga wanena mbuyanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 koma anyamata anu adzaoloka, yense wokonzekera ndi zankhondo pamaso pa Yehova kunkhondo, monga wanena mbuyanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Koma atumiki anufe, tiwoloka aliyense atatenga zida, kukamenya nkhondo pamaso pa Chauta, monga momwe inu mbuyathu mwalamulira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 koma antchito anufe, mwamuna aliyense amene ali ndi chida cha nkhondo, adzawoloka kukamenya nkhondo pamaso pa Yehova monga mbuye wathu wanenera.” Onani mutuwo |